Maliro 2:7 - Buku Lopatulika7 Ambuye wataya guwa lake la nsembe, malo ake opatulika amnyansira; wapereka m'manja a adani ake makoma a zinyumba zake; iwo anapokosera m'nyumba ya Yehova ngati tsiku la msonkhano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ambuye wataya guwa lake la nsembe, malo ake opatulika amnyansira; wapereka m'manja a adani ake makoma a zinyumba zake; iwo anaphokosera m'nyumba ya Yehova ngati tsiku la msonkhano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Chauta adanyoza ngakhale guwa lake lomwe, ndipo adaŵakana malo ake opatulika. Adapereka malinga a nyumba zake zachifumu m'manja mwa adani ake. M'nyumba yeniyeni ya Chauta adaniwo adafuula ndi chimwemwe monga momwe zimachitikira pa tsiku lachikondwerero. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ambuye wakana guwa lake la nsembe ndipo wasiya malo ake opatulika. Iye wapereka makoma a nyumba zake zaufumu kwa mdani wake; adaniwo anafuwula mʼnyumba ya Yehova ngati kuti ndi pa tsiku la chikondwerero. Onani mutuwo |