Maliro 2:5 - Buku Lopatulika5 Ambuye wasanduka mdani, wameza Israele; wameza zinyumba zake zonse, wapasula malinga ake; nachulukitsira mwana wamkazi wa Yuda maliro ndi chibumo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Yehova wasanduka mdani, wameza Israele; wameza zinyumba zake zonse, wapasula malinga ake; nachulukitsira mwana wamkazi wa Yuda maliro ndi chibumo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Chauta adakhala ngati mdani, adaononga Israele. Adaononga nyumba zonse zachifumu, malinga ao onse adaŵasandutsa mabwinja. Adachulukitsa kulira ndi kudandaula pakati pa anthu a ku Yuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ambuye ali ngati mdani; wawonongeratu Israeli; wawonongeratu nyumba zake zonse zaufumu ndipo wawononga malinga ake. Iye wachulukitsa kubuma ndi kulira kwa mwana wamkazi wa Yuda. Onani mutuwo |