Maliro 2:18 - Buku Lopatulika18 Mtima wao unafuula kwa Ambuye, linga iwe la mwana wamkazi wa Ziyoni, igwe misozi ngati mtsinje usana ndi usiku; usapume kanthawi, asaleke mwana wa diso lako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Mtima wao unafuula kwa Ambuye, linga iwe la mwana wamkazi wa Ziyoni, igwe misozi ngati mtsinje usana ndi usiku; usapume kanthawi, asaleke mwana wa diso lako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Fuulani kwamphamvu kwa Ambuye, inu anthu a ku Ziyoni. Misozi yanu ichite kuti yoyoyo, ngati mtsinje, usana ndi usiku. Musadzipatse nthaŵi yoti mupumule. Misozi yanu isalekeze. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Mitima ya anthu ikufuwulira Ambuye. Iwe khoma la mwana wamkazi wa Ziyoni, misozi yako itsike ngati mtsinje usana ndi usiku; usadzipatse wekha mpumulo, maso ako asaleke kukhetsa misozi. Onani mutuwo |