Maliro 2:13 - Buku Lopatulika13 Ndikuchitire umboni wotani? Ndikuyerekeze ndi chiyani, mwana wamkazi wa Yerusalemu? Ndikulinganize ndi chiyani kuti ndikutonthoze, namwaliwe, mwana wamkazi wa Ziyoni? Popeza akula ngati nyanja; ndani angakuchize? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndikuchitire umboni wotani? Ndikuyerekeze ndi chiyani, mwana wamkazi wa Yerusalemu? Ndikulinganize ndi chiyani kuti ndikutonthoze, namwaliwe, mwana wamkazi wa Ziyoni? Popeza akula ngati nyanja; ndani angakuchize? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Iwe mzinda wa Yerusalemu, ndinganene chiyani za iwe, kaya nkukuyerekeza ndi chiyani? Iwe mzinda wangwiro wa Ziyoni, kodi ndingakufanizire ndi yani, kuti choncho ndikusangalatse? Kuwonongeka kwako nkwakukulu ngati nyanja. Ndani angathe kukukonzanso? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndinganene chiyani za iwe? Ndingakufanizire ndi chiyani, iwe mwana wamkazi wa Yerusalemu? Kodi ndingakufanizire ndi yani kuti ndikutonthoze, iwe namwali wa Ziyoni? Chilonda chako ndi chozama ngati nyanja, kodi ndani angakuchiritse? Onani mutuwo |