Maliro 2:12 - Buku Lopatulika12 Amati kwa amao, Tirigu ndi vinyo ali kuti? Pokomoka iwo ngati olasidwa m'makwalala a mzindawu, potsanulidwa miyoyo yao pa zifuwa za amao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Amati kwa amao, Tirigu ndi vinyo ali kuti? Pokomoka iwo ngati olasidwa m'makwalala a mudziwu, potsanulidwa miyoyo yao pa zifuwa za amao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Anawo akufunsa amai ao kuti, “Kodi chakudya ndi chakumwa tingazipeze kuti?” Akufunsa zimenezi pamene akukomoka m'miseu yamumzinda ngati anthu olasidwa. Akuthatha ndi moyo pa mfukato wa amai ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Anawo akufunsa amayi awo kuti, “Kodi tirigu ndi vinyo zili kuti?” pamene akukomoka ngati anthu olasidwa mʼmisewu ya mʼmizinda, pamene miyoyo yawo ikufowoka mʼmanja mwa amayi awo. Onani mutuwo |