Maliro 2:11 - Buku Lopatulika11 Maso anga alefuka ndi misozi, m'kati mwanga mugwedezeka; chiwindi changa chagwa pansi chifukwa cha kupasuka kwa mwana wamkazi wa anthu a mtundu wanga; chifukwa tiana ndi oyamwa akomoka m'makwalala a mzindawu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Maso anga alefuka ndi misozi, m'kati mwanga mugwedezeka; chiwindi changa chagwa pansi chifukwa cha kupasula kwa mwana wamkazi wa anthu a mtundu wanga; chifukwa tiana ndi oyamwa akomoka m'makwalala a mudziwu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Maso anga atopa nkulira, moyo wanga wazunzika zedi, Mumtima mwanga mwadzaza chisoni, chifukwa choti anthu anga aonongeka, ana ndi makanda omwe akukomoka m'miseu yamumzinda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Maso anga atopa ndi kulira, ndazunzika mʼmoyo mwanga, mtima wanga wadzaza ndi chisoni chifukwa anthu anga akuwonongeka, chifukwa ana ndi makanda akukomoka mʼmisewu ya mu mzinda. Onani mutuwo |