Maliro 1:8 - Buku Lopatulika8 Yerusalemu wachimwa kwambiri; chifukwa chake wasanduka chinthu chonyansa; onse akuulemekeza aupeputsa, pakuti auona wamaliseche; inde, uusa moyo, nubwerera m'mbuyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Yerusalemu wachimwa kwambiri; chifukwa chake wasanduka chinthu chonyansa; onse akuulemekeza aupeputsa, pakuti auona wamaliseche; inde, uusa moyo, nubwerera m'mbuyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Yerusalemu adachimwa kwambiri, motero wasanduka wonyansa. Onse amene ankamulemekeza, akumunyoza tsopano, chifukwa aona maliseche ake. Iyeyo akungobuula ndipo akuyang'ana kumbali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Yerusalemu wachimwa kwambiri ndipo potero wakhala wodetsedwa. Onse amene ankamulemekeza pano akumunyoza, chifukwa aona umaliseche wake. Iye mwini akubuwula ndipo akubisa nkhope yake. Onani mutuwo |