Maliro 1:6 - Buku Lopatulika6 Ulemu wake wonse wamchokera mwana wamkazi wa Ziyoni; akalonga ake asanduka nswala zosapeza busa, anayenda opanda mphamvu pamaso pa wompirikitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ulemu wake wonse wamchokera mwana wamkazi wa Ziyoni; akalonga ake asanduka nswala zosapeza busa, anayenda opanda mphamvu pamaso pa wompirikitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ulemerero wonse wa Ziyoni wachokeratu. Akalonga ake asanduka ngati mphoyo zosoŵa msipu. Ankathaŵa opanda ndi mphamvu zomwe, pofika adani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ulemerero wonse wa mwana wamkazi wa Ziyoni wachokeratu. Akalonga ake ali ngati mbawala zosowa msipu; alibe mphamvu zothawira owathamangitsa. Onani mutuwo |