Maliro 1:5 - Buku Lopatulika5 Amaliwongo ake asanduka akulu ake, adani ake napindula; pakuti Yehova wamsautsa pochuluka zolakwa zake; ana ake aang'ono alowa m'ndende pamaso pa adani ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Amaliwongo ake asanduka akulu ake, adani ake napindula; pakuti Yehova wamsautsa pochuluka zolakwa zake; ana ake ang'ono alowa m'ndende pamaso pa adani ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adani ake asanduka omulamulira, odana naye akupeza bwino, popeza kuti Chauta wamugwetsa m'mavuto chifukwa cha machimo ochuluka a anthu ake. Ana ake amuchokera, atengedwa ukapolo ndi adani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Adani ake asanduka mabwana ake; odana naye akupeza bwino. Yehova wamubweretsera mavuto chifukwa cha machimo ake ambiri. Ana ake atengedwa ukapolo pamaso pa mdani. Onani mutuwo |