Maliro 1:16 - Buku Lopatulika16 Chifukwa cha zimenezi ndilira; diso langa, diso langatu likudza madzi: Pakuti wonditonthoza, wotsitsimutsa moyo wanga, anditalikira; ana anga asungulumwa, pakuti adaniwo apambana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Chifukwa cha zimenezi ndilira; diso langa, diso langatu likudza madzi: Pakuti wonditonthoza, wotsitsimutsa moyo wanga, anditalikira; ana anga asungulumwa, pakuti adaniwo apambana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Chifukwa cha zimenezi ndikulira, misozi ili mbwembwembwe m'masomu. Pakuti wondisangalatsa sali pafupi, wondilimbitsa mtima ali kutali. Anthu anga asiyidwa chifukwa mdani watigonjetsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 “Chifukwa cha zimenezi ndikulira ndipo maso anga adzaza ndi misozi. Palibe aliyense pafupi woti anditonthoze, palibe aliyense wondilimbitsa mtima. Ana anga ali okhaokha chifukwa mdani watigonjetsa. Onani mutuwo |