Maliro 1:13 - Buku Lopatulika13 Anatumiza moto wochokera kumwamba kulowa m'mafupa anga, unawagonjetsa; watchera mapazi anga ukonde, wandibwezera m'mbuyo; wandipululutsa ndi kundilefula tsiku lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Anatumiza moto wochokera kumwamba kulowa m'mafupa anga, unawagonjetsa; watchera mapazi anga ukonde, wandibwezera m'mbuyo; wandipululutsa ndi kundilefula tsiku lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Adatumiza moto kuchokera Kumwamba. Udaloŵa mpaka m'kati mwa mafupa anga. Adayala ukonde kuti akole mapazi anga, nandibweza. Adandisiya ndili ndi chisoni chachikulu, ndili wolefuka tsiku lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 “Anatumiza moto kuchokera kumwamba, unalowa mpaka mʼmafupa anga. Anayala ukonde kuti ukole mapazi anga ndipo anandibweza. Anandisiya wopanda chilichonse, wolefuka tsiku lonse. Onani mutuwo |