Maliro 1:12 - Buku Lopatulika12 Kodi muyesa chimenechi chabe, nonsenu opita panjira? Penyani nimuone, kodi chilipo chisoni china ngati changachi amandimvetsa ine, chimene Yehova wandisautsa nacho tsiku la mkwiyo wake waukali? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Kodi muyesa chimenechi chabe, nonsenu opita panjira? Penyani nimuone, kodi chilipo chisoni china ngati changachi amandimvetsa ine, chimene Yehova wandisautsa nacho tsiku la mkwiyo wake waukali? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Kodi zimenezi mukuziyesa zachabe, inu amene mukudutsanu? Tangopenyani, muwone ngati pali mavuto ena onga angaŵa, mavuto amene Chauta adandigwetsamo, pamene adandikwiyira koopsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Kodi zimenezi mukuziyesa zachabe, inu nonse mukudutsa? Yangʼanani ndipo muone. Kodi pali mavuto ofanana ndi amene andigwerawa, amene Ambuye anandibweretsera pa tsiku la ukali wake? Onani mutuwo |