Maliro 1:11 - Buku Lopatulika11 Anthu ake onse ausa moyo nafunafuna mkate; ndi zokondweretsa zao agula zakudya kuti atsitsimutse moyo wao; taonani, Yehova, nimupenye; pakuti ndasanduka wonyansa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Anthu ake onse ausa moyo nafunafuna mkate; ndi zokondweretsa zao agula zakudya kuti atsitsimutse moyo wao; taonani, Yehova, nimupenye; pakuti ndasanduka wonyansa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Anthu ake onse amabuula akamafunafuna chakudya. Chuma chao amagulitsana ndi chakudya, kuti apezenso mphamvu. Akuti, “Inu Chauta penyani, muwone m'mene akundinyozera.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Anthu ake onse akubuwula pamene akufunafuna chakudya; asinthanitsa chuma chawo ndi chakudya kuti akhale ndi moyo. “Inu Yehova, taonani ndipo ganizirani, chifukwa ine ndanyozeka.” Onani mutuwo |