Maliro 1:10 - Buku Lopatulika10 Amaliwongo atambasulira manja ao pa zokondweretsa zake zonse; pakuti waona amitundu atalowa m'malo ake opatulika, amene munalamulira kuti asalowe mumsonkhano mwanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Amaliwongo atambasulira manja ao pa zokondweretsa zake zonse; pakuti waona amitundu atalowa m'malo ake opatulika, amene munalamulira kuti asalowe mumsonkhano mwanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Adani adamulanda chuma chake chonse. M'malo ake oyera mudaloŵa anthu a mitundu ina, amene Inu Chauta mudaŵaletsa kuloŵa mumsonkhano mwanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Adani amulanda chuma chake chonse; iye anaona mitundu ya anthu achikunja ikulowa mʼmalo ake opatulika, amene Inu Mulungu munawaletsa kulowa mu msonkhano wanu. Onani mutuwo |