Malaki 3:18 - Buku Lopatulika18 Pamenepo mudzabwera ndi kuzindikira pakati pa wolungama ndi woipa, pakati pa iye wotumikira Mulungu ndi iye wosamtumikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pamenepo mudzabwera ndi kuzindikira pakati pa wolungama ndi woipa, pakati pa iye wotumikira Mulungu ndi iye wosamtumikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Pamenepo mudzaonanso kusiyana pakati pa anthu abwino ndi anthu oipa, pakati pa anthu otumikira Mulungu ndi osamtumikira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pamenepo mudzaonanso kusiyana pakati pa anthu olungama ndi oyipa, pakati pa amene amatumikira Mulungu ndi amene satumikira Mulungu.” Onani mutuwo |