Malaki 3:13 - Buku Lopatulika13 Mau anu andilimbira, ati Yehova. Koma inu mukuti, Tanena motsutsana nanu ndi chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Mau anu andilimbira, ati Yehova. Koma inu mukuti, Tanena motsutsana nanu ndi chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Chauta akunena kuti, “Mwalankhula mau olasa onena Ine. Komabe mukuti, ‘Kodi takunenani zotani?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Yehova akuti, “Mwayankhula mawu owawa onena za Ine. “Komabe inu mukufunsa kuti, ‘Kodi tanena chiyani chotsutsana nanu?’ Onani mutuwo |