Malaki 3:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo amitundu onse adzatcha inu odala; pakuti mudzakhala dziko lokondweretsa, ati Yehova wa makamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo amitundu onse adzatcha inu odala; pakuti mudzakhala dziko lokondweretsa, ati Yehova wa makamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Motero anthu a mitundu yonse adzakutchulani odala, pakuti dziko lanu lidzakhala lokondweretsa. Ndikutero Ine Chauta Wamphamvuzonse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Motero anthu amitundu yonse adzakutchulani odala, pakuti dziko lanu lidzakhala lokondweretsa,” akutero Yehova Wamphamvuzonse. Onani mutuwo |