Malaki 2:12 - Buku Lopatulika12 Yehova adzalikha munthu wakuchita ichi, wogalamutsa ndi wovomereza m'mahema a Yakobo, ndi iye wopereka chopereka kwa Yehova wa makamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Yehova adzalikha munthu wakuchita ichi, wogalamutsa ndi wovomereza m'mahema a Yakobo, ndi iye wopereka chopereka kwa Yehova wa makamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Wina aliyense wochita zimenezi Chauta amchotse ku banja la Yakobe. Asakhale nawonso ndi anthu opereka nsembe kwa Chauta Wopambanazonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndipo wina aliyense wochita zimenezi, kaya munthuyo ndi wotani, Yehova amuchotse ku banja la Yakobo, ngakhale atabweretsa zopereka kwa Yehova Wamphamvuzonse. Onani mutuwo |