Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 9:42 - Buku Lopatulika

42 Ndipo kudadziwika ku Yopa konse: ndipo ambiri anakhulupirira Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

42 Ndipo kudadziwika ku Yopa konse: ndipo ambiri anakhulupirira Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

42 Anthu onse a ku Yopa adamva zimenezi, ndipo ambiri adakhulupirira Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

42 Zimenezi zinadziwika ku Yopa konse, ndipo anthu ambiri anakhulupirira Ambuye.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 9:42
17 Mawu Ofanana  

ndipo ife tidzatema mitengo ku Lebanoni monga mwa kusowa kwanu konse; ndipo tidzabwera nayo kwa inu yoyandamitsa paphaka kufikira ku Yopa; ndipo inu mudzakwera nayo ku Yerusalemu.


Koma Yona ananyamuka kuti athawire ku Tarisisi, kuzemba Yehova; ndipo anatsikira ku Yopa, napezako chombo chomuka ku Tarisisi, napereka ndalama zake, natsikira m'menemo, kuti apite nao ku Tarisisi kuzemba Yehova.


Koma Yesu pamene anamva, anati, Kudwala kumene sikuli kwa imfa, koma chifukwa cha ulemerero wa Mulungu, kuti Mwana wa Mulungu alemekezedwe nako.


Chifukwa chake ambiri a mwa Ayuda amene anadza kwa Maria, m'mene anaona chimene anachita, anakhulupirira Iye.


pakuti ambiri a Ayuda anachoka chifukwa cha iye, nakhulupirira Yesu.


Koma Yesu anafuula nati, Iye wokhulupirira Ine, sakhulupirira Ine, koma Iye wondituma Ine.


Ndipo tsopano tumiza amuna ku Yopa, aitane munthu Simoni, wotchedwanso Petro;


ndipo m'mene adawafotokozera zonse, anawatuma ku Yopa.


ndipo anatiuza ife kuti adaona mngelo wakuimirira m'nyumba yake, ndi kuti, Tumiza anthu ku Yopa, akaitane Simoni, wonenedwanso Petro;


Ndipo dzanja la Ambuye linali nao; ndi unyinji wakukhulupirira unatembenukira kwa Ambuye.


Ndinali ine m'mzinda wa Yopa ndi kupemphera; ndipo m'kukomoka ndinaona masomphenya, chotengera chilikutsika, ngati chinsalu chachikulu chogwiridwa pangodya zake zinai; ndi kutsika kumwamba, ndipo chinadza pali ine;


Ndipo anamuona iye onse akukhala ku Lida ndi ku Saroni, natembenukira kwa Ambuye amenewa.


Koma mu Yopa munali wophunzira dzina lake Tabita, ndilo kunena Dorika; mkazi ameneyo anadzala ndi ntchito zabwino ndi zachifundo zimene anazichita.


Ndipo popeza Lida ndi pafupi pa Yopa, m'mene anamva ophunzirawo kuti Petro anali pomwepo, anamtumizira anthu awiri, namdandaulira, Musachedwa mudze kwa ife.


Ndipo kunali, kuti anakhala iye mu Yopa masiku ambiri ndi munthu Simoni wofufuta zikopa.


ndi Meyarikoni, ndi Rakoni, ndi malire pandunji pa Yopa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa