Machitidwe a Atumwi 9:32 - Buku Lopatulika32 Koma kunali, pakupita Petro ponseponse, anatsikiranso kwa oyera mtima akukhala ku Lida. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Koma kunali, pakupita Petro ponseponse, anatsikiranso kwa oyera mtima akukhala ku Lida. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Pamene Petro ankayendera anthu a Mulungu uku ndi uku, adakafika kwa amene ankakhala ku Lida. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Pamene Petro amayendera mpingo, anapita kukachezera oyera mtima a ku Luda. Onani mutuwo |