Machitidwe a Atumwi 9:30 - Buku Lopatulika30 Koma m'mene abale anachidziwa, anapita naye ku Kesareya, namtumiza achokeko kunka ku Tariso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Koma m'mene abale anachidziwa, anapita naye ku Kesareya, namtumiza achokeko kunka ku Tariso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Pamene abale adamva zimenezi, adapita naye ku Kesareya namtumiza ku Tariso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Abale atadziwa zimenezi, anamutenga Saulo ndi kupita naye ku Kaisareya, ndipo anamutumiza ku Tarisisi. Onani mutuwo |