Machitidwe a Atumwi 9:29 - Buku Lopatulika29 ndipotu analankhula natsutsana ndi Agriki; koma anayesayesa kumupha iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 nanena molimbika mtima m'dzina la Ambuye; ndipotu analankhula natsutsana ndi Agriki; koma anayesayesa kumupha iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Ankalankhulanso ndi kumatsutsana ndi Ayuda olankhula Chigriki, koma iwowo ankafunafuna kumupha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Anayankhula ndi kutsutsana ndi Ayuda a Chihelene, koma iwo ankafuna kumupha. Onani mutuwo |