Machitidwe a Atumwi 9:26 - Buku Lopatulika26 Koma m'mene anafika ku Yerusalemu, anayesa kudziphatika kwa ophunzira; ndipo anamuopa iye onse, osakhulupirira kuti ali wophunzira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Koma m'mene anafika ku Yerusalemu, anayesa kudziphatika kwa ophunzira; ndipo anamuopa iye onse, osakhulupirira kuti ali wophunzira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Saulo atafika ku Yerusalemu, adayesa kuloŵa m'gulu la ophunzira aja. Koma onse adachita naye mantha, osakhulupirira kuti nayenso ndi wophunzira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Saulo atafika ku Yerusalemu, anayesetsa kulowa mʼgulu la ophunzira koma onse anamuopa chifukwa sanakhulupirire kuti anali wophunziradi. Onani mutuwo |