Machitidwe a Atumwi 9:24 - Buku Lopatulika24 koma chiwembu chao chinadziwika ndi Saulo. Ndipo anadikiranso pazipata usana ndi usiku kuti amuphe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 koma chiwembu chao chinadziwika ndi Saulo. Ndipo anadikiranso pazipata usana ndi usiku kuti amuphe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 koma anthu ena adamuuzako za chiwembucho. Anthu achiwembuwo ankadikira pa zipata za linga la mzinda usana ndi usiku kuti amuphe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 koma iye anadziwa za chiwembucho. Anthu ankadikirira usana ndi usiku pa zipata za mzindawo kuti amuphe. Onani mutuwo |