Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 9:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo atapita masiku ambiri, Ayuda anapangana kuti amuphe iye;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo atapita masiku ambiri, Ayuda anapangana kuti amuphe iye;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Patapita masiku ambiri, Ayuda adapangana kuti aphe Saulo,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Patapita masiku ambiri, Ayuda anapangana zoti aphe Saulo,

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 9:23
14 Mawu Ofanana  

Koma Ayuda anakakamiza akazi opembedza ndi omveka, ndi akulu a mzindawo, nawautsira chizunzo Paulo ndi Barnabasi, ndipo anawapirikitsa iwo m'malire ao.


Ndipo anafika kumeneko Ayuda kuchokera ku Antiokeya ndi Ikonio; nakopa makamu, ndipo anamponya Paulo miyala, namguzira kunja kwa mzinda; namuyesa kuti wafa.


Koma Ayuda osamvera anautsa mitima ya Agriki kuti aipse abale athu.


anthu amene anapereka moyo wao chifukwa cha dzina la Yesu Khristu Ambuye wathu.


Ndipo m'mene adakhalako miyezi itatu, ndipo atampangira chiwembu Ayuda, poti iye apite ndi ngalawa ku Siriya, anatsimikiza mtima abwerere popyola Masedoniya.


Ndipo kutacha, Ayuda anapangana chiwembu, nadzitemberera, ndi kunena kuti sadzadya kapena kumwa kanthu, kufikira atamupha Paulo;


pakuti Ine ndidzamuonetsa iye zinthu zambiri ayenera iye kuzimva kuwawa chifukwa cha dzina langa.


Koma Saulo anakula makamaka mumphamvu, nadodometsa Ayuda akukhala mu Damasiko, nawatsimikizira kuti ameneyo ndi Khristu.


paulendo kawirikawiri, moopsa mwake mwa mitsinje, moopsa mwake mwa olanda, moopsa modzera kwa mtundu wanga, moopsa modzera kwa amitundu, moopsa m'mzinda, moopsa m'chipululu, moopsa m'nyanja, moopsa mwa abale onyenga;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa