Machitidwe a Atumwi 9:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo onse amene anamva anadabwa, nanena, Suyu iye amene anaononga mu Yerusalemu onse akuitana pa dzina ili? Ndipo wadza kuno kudzatero, kuti amuke nao omangidwa kwa ansembe aakulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo onse amene anamva anadabwa, nanena, Suyu iye amene anaononga m'Yerusalemu onse akuitana pa dzina ili? Ndipo wadza kuno kudzatero, kuti amuke nao omangidwa kwa ansembe aakulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Anthu onse amene ankamva mau akewo ankadabwa, namafunsana kuti, “Kodi ameneyu si yemwe uja amene ku Yerusalemu ankapha anthu otama dzinali mopemba? Kodi siwabwera kuno kuti aŵamange otereŵa ndi kukaŵapereka kwa akulu a ansembe?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Onse amene anamva iye akulalikira anadabwa ndipo anafunsa kuti, “Kodi uyu si munthu amene anayambitsa kuzunza okhulupirira ku mpingo wa ku Yerusalemu? Kodi siwabwera kuno kuti awamange ndi kuwapereka kwa akulu a ansembe?” Onani mutuwo |