Machitidwe a Atumwi 9:19 - Buku Lopatulika19 ndipo analandira chakudya, naona nacho mphamvu. Ndipo anakhala pamodzi ndi ophunzira a ku Damasiko masiku ena. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 ndipo analandira chakudya, naona nacho mphamvu. Ndipo anakhala pamodzi ndi ophunzira a ku Damasiko masiku ena. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 ndipo atadya chakudya, adapezanso mphamvu. Saulo adakhala masiku angapo limodzi ndi ophunzira a ku Damasiko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 ndipo atadya chakudya, anapezanso mphamvu. Saulo anakhala masiku angapo ndi ophunzira a ku Damasiko. Onani mutuwo |