Machitidwe a Atumwi 9:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo pomwepo padagwa kuchoka m'maso mwake ngati mamba, ndipo anapenyanso; ndipo ananyamuka nabatizidwa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo pomwepo padagwa kuchoka m'maso mwake ngati mamba, ndipo anapenyanso; ndipo ananyamuka nabatizidwa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Pompo m'maso mwake mudachoka zinthu zonga mamba a nsomba, ndipo adayambanso kupenya. Adaimirira nabatizidwa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Nthawi yomweyo mʼmaso mwa Saulo munachoka zinthu zokhala ngati mamba ansomba, ndipo anayambanso kuona. Iye anayimirira nabatizidwa, Onani mutuwo |