Machitidwe a Atumwi 9:16 - Buku Lopatulika16 pakuti Ine ndidzamuonetsa iye zinthu zambiri ayenera iye kuzimva kuwawa chifukwa cha dzina langa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 pakuti Ine ndidzamuonetsa iye zinthu zambiri ayenera iye kuzimva kuwawa chifukwa cha dzina langa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ine ndidzamuwonetsa zoŵaŵa zonse zimene adzayenera kumva chifukwa cha Ine.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ine ndidzamuonetsa zowawa zonse zimene ayenera kumva chifukwa cha dzina langa.” Onani mutuwo |