Machitidwe a Atumwi 9:14 - Buku Lopatulika14 ndi kuti pano ali nao ulamuliro wa kwa ansembe aakulu wakumanga onse akuitana pa dzina lanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 ndi kuti pano ali nao ulamuliro wa kwa ansembe aakulu wakumanga onse akuitana pa dzina lanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ndipo wabwera kuno ndi ulamuliro wa akulu a ansembe kuti adzamange onse otama dzina lanu mopemba.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndipo wabwera kuno ndi ulamuliro wa akulu ansembe kuti adzamange onse amene amayitana pa dzina lanu.” Onani mutuwo |