Machitidwe a Atumwi 8:40 - Buku Lopatulika40 Koma Filipo anapezedwa ku Azoto; ndipo popitapita analalikira Uthenga Wabwino m'midzi yonse, kufikira anadza iye ku Kesareya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Koma Filipo anapezedwa ku Azoto; ndipo popitapita analalikira Uthenga Wabwino m'midzi yonse, kufikira anadza iye ku Kesareya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Tsono Filipo adapezeka kuti ali ku Azoto. Adapita m'dziko monse akulalika Uthenga Wabwino m'mizinda yonse, mpaka adakafika ku Kesareya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Koma Filipo anapezeka kuti ali ku Azoto ndipo anazungulira konse, kulalikira Uthenga Wabwino mʼmizinda yonse mpaka anakafika ku Kaisareya. Onani mutuwo |