Machitidwe a Atumwi 8:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo pamene anakwera kutuluka m'madzi, Mzimu wa Ambuye anakwatula Filipo; ndipo mdindo sanamuonenso, pakuti anapita njira yake wokondwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo pamene anakwera kutuluka m'madzi, Mzimu wa Ambuye anakwatula Filipo; ndipo mdindo sanamuonanso, pakuti anapita njira yake wokondwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Pamene adatuluka m'madzimo, Mzimu wa Ambuye adamchotsapo Filipo uja. Ndipo nduna ija siidamuwonenso, koma idapitirira ulendo wake ikusangalala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Pamene iwo anatuluka mʼmadzimo, Mzimu wa Ambuye anamukwatula Filipo, ndipo Ndunayo sinamuonenso, koma inapitiriza ulendo wake ikusangalala. Onani mutuwo |