Machitidwe a Atumwi 8:36 - Buku Lopatulika36 Ndipo monga anapita panjira pao, anadza kumadzi akuti; ndipo mdindoyo anati, Taonapo madzi; chindiletsa ine chiyani ndisabatizidwe? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ndipo monga anapita panjira pao, anadza kumadzi akuti; ndipo mdindoyo anati, Taonapo madzi; chindiletsa ine chiyani ndisabatizidwe? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Ndipo pamene ankapita mumseumo, adafika pena pamene panali madzi. Nduna ija idati, “Madzi si aŵa. Monga pali choletsa kuti ndisabatizidwe?” [ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Akuyenda mu msewu anafika pamalo pamene panali madzi ndipo ndunayo inati, “Taonani madzi awa. Kodi pali chondiletsa kuti ndibatizidwe?” Onani mutuwo |