Machitidwe a Atumwi 8:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo mdindoyo anayankha Filipo, nati, Ndikupempha, mneneri anena ichi za yani? Za yekha, kapena za wina? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo mdindoyo anayankha Filipo, nati, Ndikupempha, mneneri anena ichi za yani? Za yekha, kapena za wina? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Pamenepo nduna ija idati, “Pepani, tandiwuzani, kodi zimenezi mneneriyo akunena za yani, za iye mwini, kapena za wina?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Ndunayo inamufunsa Filipo kuti, “Chonde, uzeni, kodi mneneri akuyankhula za ndani, za iye mwini kapena za munthu wina?” Onani mutuwo |