Machitidwe a Atumwi 8:31 - Buku Lopatulika31 Koma anati, Ndingathe bwanji, popanda munthu wonditsogolera ine? Ndipo anapempha Filipo akwere nakhale naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Koma anati, Ndingathe bwanji, popanda munthu wonditsogolera ine? Ndipo anapempha Filipo akwere nakhale naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Iye adati, “Ha, ndingamvetse bwanji popanda wina wondimasulira?” Motero adaitana Filipo kuti adzakwere ndi kukhala naye pagaletapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Iye anayankha kuti, “Ndingamvetse bwanji popanda wina wondimasulira?” Ndipo iye anayitana Filipo kuti abwere ndikukhala naye mʼgaleta. Onani mutuwo |