Machitidwe a Atumwi 8:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo Mzimu anati kwa Filipo, Yandikira, nudziphatike kugaleta uyu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo Mzimu anati kwa Filipo, Yandikira, nudziphatike kugaleta uyu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Tsono Mzimu Woyera adauza Filipo kuti, “Pita, kayandikane nalo galetalo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Mzimu anamuwuza Filipo kuti, “Pita pa galeta ilo ndipo ukakhale pafupi nalo.” Onani mutuwo |