Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 8:28 - Buku Lopatulika

28 ndipo analinkubwerera, nalikukhala pa galeta wake, nawerenga mneneri Yesaya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 ndipo analinkubwerera, nalikukhala pa galeta wake, nawerenga mneneri Yesaya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Nthaŵi imeneyo ankabwerera kwao. Anali pa galeta akuŵerenga buku la mneneri Yesaya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 ndipo akubwerera kwawo atakwera pa galeta lake amawerenga buku la mneneri Yesaya.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 8:28
19 Mawu Ofanana  

Ndinalandira mboni zanu zikhale cholandira chosatha; pakuti ndizo zokondweretsa mtima wanga.


Ndili nayo nzeru yakuposa aphunzitsi anga onse; pakuti ndilingalira mboni zanu.


Masomphenya a Yesaya mwana wa Amozi, amene iye anaona, onena za Yuda ndi Yerusalemu, masiku a Uziya, Yotamu, Ahazi, ndi Hezekiya, mafumu a Yuda.


monga mwalembedwa m'buku la Yesaya mneneri, kuti, Mau a wofuula m'chipululu, konzani khwalala la Ambuye, lungamitsani njira zake.


Ndipo anapereka kwa Iye buku la Yesaya mneneri. Ndipo m'mene Iye adafunyulula bukulo, anapeza pomwe panalembedwa,


Koma popeza sanavomerezane, anachoka atanena Paulo mau amodzi, kuti, Mzimu Woyera analankhula kokoma mwa Yesaya Mneneri kwa makolo anu,


Ndipo ananyamuka napita; ndipo taona munthu wa ku Etiopiya, mdindo wamphamvu wa Kandake, mfumu yaikazi ya Aetiopiya, ndiye wakusunga chuma chake chonse, amene anadza ku Yerusalemu kudzapemphera;


Ndipo Mzimu anati kwa Filipo, Yandikira, nudziphatike kugaleta uyu.


Mau a Khristu akhalitse mwa inu chichulukire mu nzeru yonse, ndi kuphunzitsa ndi kuyambirirana eni okha ndi masalimo, ndi mayamiko ndi nyimbo zauzimu, ndi kuimbira Mulungu ndi chisomo mumtima mwanu.


Buku ili la chilamulo lisachoke pakamwa pako; koma ulingiriremo usana ndi usiku, kuti usamalire kuchita monga mwa zonse zolembedwamo; popeza ukatero udzakometsa njira yako, nudzachita mwanzeru.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa