Machitidwe a Atumwi 8:25 - Buku Lopatulika25 Pamenepo iwo, atatha kuchita umboni ndi kulankhula mau a Ambuye, anabwera kunka ku Yerusalemu, nalalikira Uthenga Wabwino kumidzi yambiri ya Asamariya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Pamenepo iwo, atatha kuchita umboni ndi kulankhula mau a Ambuye, anabwera kunka ku Yerusalemu, nalalikira Uthenga Wabwino kumidzi yambiri ya Asamariya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Petro ndi Yohane atatha kupereka umboni wao ndi kulalika mau a Ambuye, adabwerera ku Yerusalemu. Ankapita nalalika Uthenga Wabwino m'midzi yambiri ya Asamariya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Atatha kuchitira umboni ndi kulalikira mawu a Ambuye, Petro ndi Yohane anabwerera ku Yerusalemu, atalalikira Uthenga Wabwino mʼmidzi yambiri ya Asamariya. Onani mutuwo |