Machitidwe a Atumwi 8:23 - Buku Lopatulika23 Pakuti ndiona kuti wagwidwa ndi ndulu yowawa ndi nsinga ya chosalungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Pakuti ndiona kuti wagwidwa ndi ndulu yowawa ndi nsinga ya chosalungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Pakuti ndakuwona kuti ndiwe wodzaza ndi ndulu yoŵaŵa, ndiponso ndiwe womangidwa ndi maunyolo a zoipa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Pakuti ine ndikuona kuti ndiwe wowawidwa mtima ndiponso kapolo wa tchimo.” Onani mutuwo |