Machitidwe a Atumwi 8:22 - Buku Lopatulika22 Chifukwa chake lapa choipa chako ichi, pemphera Ambuye, kuti kapena akukhululukire iwe cholingirira cha mtima wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Chifukwa chake lapa choipa chako ichi, pemphera Ambuye, kuti kapena akukhululukire iwe cholingirira cha mtima wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Nchifukwa chake tembenuka mtima, uleke choipa chakochi. Pempha Ambuye kuti mwina mwake nkukukhululukira maganizo a mumtima mwakoŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Lapa zoyipa zakozi ndipo upemphere kwa Ambuye. Mwina adzakukhululukira maganizo a mu mtima mwako. Onani mutuwo |