Machitidwe a Atumwi 8:21 - Buku Lopatulika21 Ulibe gawo kapena cholandira ndi mau awa; pakuti mtima wako suli wolunjika pamaso pa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ulibe gawo kapena cholandira ndi mau awa; pakuti mtima wako suli wolunjika pamaso pa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Ulibe gawo kapena malo pa ntchito imeneyi, pakuti mtima wako suli wolungama pamaso pa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Ulibe gawo kapena mbali pa utumikiwu, chifukwa mtima wako suli wolungama pamaso pa Mulungu. Onani mutuwo |