Machitidwe a Atumwi 8:20 - Buku Lopatulika20 Koma Petro anati kwa iye, Ndalama yako itayike nawe, chifukwa unalingirira kulandira mphatso ya Mulungu ndi ndalama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma Petro anati kwa iye, Ndalama yako itayike nawe, chifukwa unalingirira kulandira mphatso ya Mulungu ndi ndalama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Petro adamuyankha kuti, “Ndalama zakozo ukatayike nazo pamodzi. Iwe ukuganiza kuti ungathe kupata mphatso ya Mulungu pakupereka ndalama kodi? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Petro anayankha kuti, “Ndalama zako utayike nazo pamodzi, chifukwa unaganiza kuti ungathe kugula mphatso ya Mulungu ndi ndalama! Onani mutuwo |