Machitidwe a Atumwi 8:16 - Buku Lopatulika16 pakuti kufikira pamenepo nkuti asanagwe pa wina mmodzi wa iwo; koma anangobatizidwa m'dzina la Ambuye Yesu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 pakuti kufikira pamenepo nkuti asanagwe pa wina mmodzi wa iwo; koma anangobatizidwa m'dzina la Ambuye Yesu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Nthaŵiyo nkuti Mzimu Woyera asanafike pa wina aliyense mwa iwo. Onsewo anali atangobatizidwa m'dzina la Ambuye Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 chifukwa Mzimu Woyera anali asanafike pa wina aliyense wa iwo; anali atangobatizidwa mʼdzina la Ambuye Yesu. Onani mutuwo |