Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 8:15 - Buku Lopatulika

15 amenewo, m'mene adatsikirako, anawapempherera, kuti alandire Mzimu Woyera:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 amenewo, m'mene adatsikirako, anawapempherera, kuti alandire Mzimu Woyera:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Iwowo atafika, adayamba kupempherera okhulupirira aja kuti alandire Mzimu Woyera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Atafika anawapempherera kuti alandire Mzimu Woyera,

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 8:15
7 Mawu Ofanana  

Ndiponso ndinena kwa inu kuti ngati awiri a inu avomerezana pansi pano chinthu chilichonse akachipempha, Atate wanga wa Kumwamba adzawachitira.


ndipo anati kwa iwo, Kodi munalandira Mzimu Woyera pamene munakhulupirira? Ndipo anati, Iai, sitinamve konse kuti Mzimu Woyera waperekedwa.


Koma Petro anati kwa iwo, Lapani, batizidwani yense wa inu m'dzina la Yesu Khristu kuloza ku chikhululukiro cha machimo anu; ndipo mudzalandira mphatso ya Mzimu Woyera.


Chifukwa chake wolankhula lilime, apemphere kuti amasule.


Pakuti ndidziwa kuti ichi chidzandichitira ine chipulumutso, mwa pembedzero lanu ndi mwa kundipatsako kwa Mzimu wa Yesu Khristu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa