Machitidwe a Atumwi 8:14 - Buku Lopatulika14 Koma pamene atumwi a ku Yerusalemu anamva kuti Samariya adalandira mau a Mulungu, anawatumizira Petro ndi Yohane; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma pamene atumwi a ku Yerusalemu anamva kuti Samariya adalandira mau a Mulungu, anawatumizira Petro ndi Yohane; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Pamene atumwi okhala ku Yerusalemu adamva kuti anthu a ku Samariya alandira mau a Mulungu, adatumako Petro ndi Yohane. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Atumwi a ku Yerusalemu atamva kuti anthu a ku Samariya analandira Mawu a Mulungu, anatumiza Petro ndi Yohane. Onani mutuwo |