Machitidwe a Atumwi 8:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo anamsamalira iye, popeza nthawi yaikulu adawadabwitsa iwo ndi matsenga ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo anamsamalira iye, popeza nthawi yaikulu adawadabwitsa iwo ndi matsenga ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ankamutsata chifukwa pa nthaŵi yaitali ankaŵadodometsa ndi matsenga akewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Anthu amamutsata chifukwa kwa nthawi yayitali amawadabwitsa ndi matsenga akewo. Onani mutuwo |