Machitidwe a Atumwi 7:56 - Buku Lopatulika56 nati, Taonani, ndipenya mu Mwamba motseguka, ndi Mwana wa Munthu alikuimirira padzanja lamanja la Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201456 nati, Taonani, ndipenya m'Mwamba motseguka, ndi Mwana wa Munthu alikuimirira pa dzanja lamanja la Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa56 Tsono adati, “Onani! Ndikuwona Kumwamba kotsekuka, ndipo Mwana wa Munthu ataimirira ku dzanja lamanja la Mulungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero56 Stefano anati, “Taonani, ndikuona kumwamba kotsekuka ndiponso Mwana wa Munthu atayimirira ku dzanja la manja la Mulungu.” Onani mutuwo |