Machitidwe a Atumwi 7:48 - Buku Lopatulika48 Komatu Wamwambamwambayo sakhala m'nyumba zomangidwa ndi manja; monga mneneri anena, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Komatu Wamwambamwambayo sakhala m'nyumba zomangidwa ndi manja; monga mneneri anena, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Ngakhale zinali choncho Mulungu Wopambanazonse sakhala m'nyumba zomangidwa ndi manja, monga akunenera mneneri kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 “Komatu, Wammwambamwambayo sakhala mʼnyumba zomangidwa ndi anthu. Monga mneneri akunena kuti, Onani mutuwo |