Machitidwe a Atumwi 7:39 - Buku Lopatulika39 amene makolo athu sanafune kumvera iye, koma anamkankha achoke, nabwerera m'mbuyo mumtima mwao ku Ejipito, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 amene makolo athu sanafuna kumvera iye, koma anamkankha achoke, nabwerera m'mbuyo mumtima mwao ku Ejipito, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 “Koma makolo athu aja adakana kumumvera, m'malo mwake adamkankhira kumbali. Mitima yao idatembenukira za ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 “Koma makolo athu anakana kumumvera iye. Iwo anamukana iye ndipo mʼmitima mwawo anatembenukira ku Igupto. Onani mutuwo |