Machitidwe a Atumwi 7:37 - Buku Lopatulika37 Uyu ndi Mose uja adati kwa ana a Israele, Mulungu adzakuutsirani Mneneri wa mwa abale anu, monga ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Uyu ndi Mose uja adati kwa ana a Israele, Mulungu adzakuutsirani Mneneri wa mwa abale anu, monga ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Mose yemweyo ndiye amene adauza Aisraele kuti, ‘Mulungu adzatuma wina kuchokera mwa abale anu kuti akhale Mneneri wanu monga ine.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 “Uyu ndi Mose uja amene anati kwa Aisraeli, ‘Mulungu adzawutsa pakati pa abale anu mneneri ngati ine.’ Onani mutuwo |